×

Kodi n’chodabwitsa kwa anthu kuti Ife tidavumbulutsa chivumbulutso kwa mmodzi wa iwo 10:2 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Yunus ⮕ (10:2) ayat 2 in Chichewa

10:2 Surah Yunus ayat 2 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Yunus ayat 2 - يُونس - Page - Juz 11

﴿أَكَانَ لِلنَّاسِ عَجَبًا أَنۡ أَوۡحَيۡنَآ إِلَىٰ رَجُلٖ مِّنۡهُمۡ أَنۡ أَنذِرِ ٱلنَّاسَ وَبَشِّرِ ٱلَّذِينَ ءَامَنُوٓاْ أَنَّ لَهُمۡ قَدَمَ صِدۡقٍ عِندَ رَبِّهِمۡۗ قَالَ ٱلۡكَٰفِرُونَ إِنَّ هَٰذَا لَسَٰحِرٞ مُّبِينٌ ﴾
[يُونس: 2]

Kodi n’chodabwitsa kwa anthu kuti Ife tidavumbulutsa chivumbulutso kwa mmodzi wa iwo ponena, “Pereka chenjezo kwa anthu ndipo uwauze nkhani zabwino anthu okhulupirira kuti adzakhala ndi mpando wapamwamba kwa Ambuye wawo?” Anthu osakhulupirira adati: “Ndithudi uyu ndi wamatsenga enieni.”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: أكان للناس عجبا أن أوحينا إلى رجل منهم أن أنذر الناس وبشر, باللغة نيانجا

﴿أكان للناس عجبا أن أوحينا إلى رجل منهم أن أنذر الناس وبشر﴾ [يُونس: 2]

Khaled Ibrahim Betala
“Kodi nchodabwitsa kwa anthu kuti tamuvumbulutsira (chivumbulutso) munthu wochokera mwa iwo (yemwe ndi Muhammad {s.a.w}) kuti: “Chenjeza anthu ndipo awuze nkhani yabwino amene akhulupirira kuti iwo adzapeza ulemelero waukulu kwa Mbuye wawo?” Osakhulupirira adati: “Ndithudi uyu ndi wa matsenga (mfiti) wowonekera.’’
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek