×

Iyendiyeameneamakuyendetsanipamtundandiponso pa nyanja mpaka pamene inu muli m’ngalawa ndipo izo zimayendetsedwa ndi 10:22 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Yunus ⮕ (10:22) ayat 22 in Chichewa

10:22 Surah Yunus ayat 22 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Yunus ayat 22 - يُونس - Page - Juz 11

﴿هُوَ ٱلَّذِي يُسَيِّرُكُمۡ فِي ٱلۡبَرِّ وَٱلۡبَحۡرِۖ حَتَّىٰٓ إِذَا كُنتُمۡ فِي ٱلۡفُلۡكِ وَجَرَيۡنَ بِهِم بِرِيحٖ طَيِّبَةٖ وَفَرِحُواْ بِهَا جَآءَتۡهَا رِيحٌ عَاصِفٞ وَجَآءَهُمُ ٱلۡمَوۡجُ مِن كُلِّ مَكَانٖ وَظَنُّوٓاْ أَنَّهُمۡ أُحِيطَ بِهِمۡ دَعَوُاْ ٱللَّهَ مُخۡلِصِينَ لَهُ ٱلدِّينَ لَئِنۡ أَنجَيۡتَنَا مِنۡ هَٰذِهِۦ لَنَكُونَنَّ مِنَ ٱلشَّٰكِرِينَ ﴾
[يُونس: 22]

Iyendiyeameneamakuyendetsanipamtundandiponso pa nyanja mpaka pamene inu muli m’ngalawa ndipo izo zimayendetsedwa ndi mphepo yabwino imene iwo amasangalala nayo. Koma mphepo ya mkuntho imawafikira ndipo mafunde amadza kwa iwo kuchokera ku mbali zonse ndipo iwo amaganiza kuti yawapeza ndipo amapemphera kwa Mulungu momuyeretsera chipembedzo chake. “Ngati mutipulumutse ku mavuto awa, ife tidzakhala othokoza.”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: هو الذي يسيركم في البر والبحر حتى إذا كنتم في الفلك وجرين, باللغة نيانجا

﴿هو الذي يسيركم في البر والبحر حتى إذا كنتم في الفلك وجرين﴾ [يُونس: 22]

Khaled Ibrahim Betala
“Iye ndi Yemwe amakuyendetsani pa ntunda ndi pa nyanja; kufikira pomwe mumakhala m’zombo; ndipo zimayenda nawo (zombozo) ndi mphepo yabwino, naisangalalira. (Mwadzidzidzi) namondwe nkuzidzera (zombozo) ndipo mafunde nkuwadzera mbali zonse natsimikiza kuti azingidwa (ndi chionongeko); amampempha Allah modzipereka kwa Iye mukupempha kwawo (uku akunena): “Ngati mutipulumutsa pa ichi, tidzakhala m’gulu la oyamika (nthawi zonse)!”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek