×

Ndipo pamene Mulungu adawapulumutsa, iwo adayamba kuchita zoipa pa dziko mopanda chilungamo. 10:23 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Yunus ⮕ (10:23) ayat 23 in Chichewa

10:23 Surah Yunus ayat 23 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Yunus ayat 23 - يُونس - Page - Juz 11

﴿فَلَمَّآ أَنجَىٰهُمۡ إِذَا هُمۡ يَبۡغُونَ فِي ٱلۡأَرۡضِ بِغَيۡرِ ٱلۡحَقِّۗ يَٰٓأَيُّهَا ٱلنَّاسُ إِنَّمَا بَغۡيُكُمۡ عَلَىٰٓ أَنفُسِكُمۖ مَّتَٰعَ ٱلۡحَيَوٰةِ ٱلدُّنۡيَاۖ ثُمَّ إِلَيۡنَا مَرۡجِعُكُمۡ فَنُنَبِّئُكُم بِمَا كُنتُمۡ تَعۡمَلُونَ ﴾
[يُونس: 23]

Ndipo pamene Mulungu adawapulumutsa, iwo adayamba kuchita zoipa pa dziko mopanda chilungamo. Oh inu anthu! Zoipa zanu simuchitira wina aliyense koma inu nokha. Chimenecho ndicho chisangalalo cha moyo wa pa dziko lapansi ndipo pambuyo pake inu mudzabwerera kwa Ife ndipo tidzakuuzani zonse zomwe mumachita

❮ Previous Next ❯

ترجمة: فلما أنجاهم إذا هم يبغون في الأرض بغير الحق ياأيها الناس إنما, باللغة نيانجا

﴿فلما أنجاهم إذا هم يبغون في الأرض بغير الحق ياأيها الناس إنما﴾ [يُونس: 23]

Khaled Ibrahim Betala
“Koma akawapulumutsa, pompo akuyamba kudzitukumula ndi kuononga pa dziko popanda chowayenereza (kutero). E inu anthu! Ndithu kuononga kwanu kukubweretserani masautso inu nokha. Ndipo chisangalalo (chake) cha moyo wa dziko lapansi (nchochepa). Kenako kobwerera kwanu ndi kwa Ife, ndipo tidzakuuzani zomwe munkachita
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek