×

Ena a iwo amakumvera iwe. Kodi iwe ungawapangitse agonthi kuti amve ngakhale 10:42 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Yunus ⮕ (10:42) ayat 42 in Chichewa

10:42 Surah Yunus ayat 42 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Yunus ayat 42 - يُونس - Page - Juz 11

﴿وَمِنۡهُم مَّن يَسۡتَمِعُونَ إِلَيۡكَۚ أَفَأَنتَ تُسۡمِعُ ٱلصُّمَّ وَلَوۡ كَانُواْ لَا يَعۡقِلُونَ ﴾
[يُونس: 42]

Ena a iwo amakumvera iwe. Kodi iwe ungawapangitse agonthi kuti amve ngakhale kuti safuna kuzindikira

❮ Previous Next ❯

ترجمة: ومنهم من يستمعون إليك أفأنت تسمع الصم ولو كانوا لا يعقلون, باللغة نيانجا

﴿ومنهم من يستمعون إليك أفأنت تسمع الصم ولو كانوا لا يعقلون﴾ [يُونس: 42]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndipo mwa iwo alipo ena amene akumvetsera kwa iwe, (koma osati ndi cholinga choti adziwe). Kodi iwe ungathe kuwamveretsa agonthi, chikhalirecho nzeru alibe
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek