×

Ngati iwo akukana iwe, nena: “Ine ndili ndi ntchito zanga ndipo nanunso 10:41 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Yunus ⮕ (10:41) ayat 41 in Chichewa

10:41 Surah Yunus ayat 41 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Yunus ayat 41 - يُونس - Page - Juz 11

﴿وَإِن كَذَّبُوكَ فَقُل لِّي عَمَلِي وَلَكُمۡ عَمَلُكُمۡۖ أَنتُم بَرِيٓـُٔونَ مِمَّآ أَعۡمَلُ وَأَنَا۠ بَرِيٓءٞ مِّمَّا تَعۡمَلُونَ ﴾
[يُونس: 41]

Ngati iwo akukana iwe, nena: “Ine ndili ndi ntchito zanga ndipo nanunso muli ndi ntchito zanu. Inu muli kutali ndi zimene ndikuchita ndipo nanenso ndili kutali ndi zimene mukuchita.”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: وإن كذبوك فقل لي عملي ولكم عملكم أنتم بريئون مما أعمل وأنا, باللغة نيانجا

﴿وإن كذبوك فقل لي عملي ولكم عملكم أنتم بريئون مما أعمل وأنا﴾ [يُونس: 41]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndipo ngati apitiriza kukutsutsa, nena: “Ine ndili ndi ntchito yanga, inunso muli ndi ntchito yanu. Inu mwatalikirana nazo zimene ndikuchita, inenso ndatalikirana nazo zimene mukuchita!”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek