×

Ndithudi iwo ndi anthu amene sayembekeza kuti adzakumana nafe ndipo amasangalala ndi 10:7 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Yunus ⮕ (10:7) ayat 7 in Chichewa

10:7 Surah Yunus ayat 7 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Yunus ayat 7 - يُونس - Page - Juz 11

﴿إِنَّ ٱلَّذِينَ لَا يَرۡجُونَ لِقَآءَنَا وَرَضُواْ بِٱلۡحَيَوٰةِ ٱلدُّنۡيَا وَٱطۡمَأَنُّواْ بِهَا وَٱلَّذِينَ هُمۡ عَنۡ ءَايَٰتِنَا غَٰفِلُونَ ﴾
[يُونس: 7]

Ndithudi iwo ndi anthu amene sayembekeza kuti adzakumana nafe ndipo amasangalala ndi moyo wa m’dziko lapansi ndi kukhutitsidwa nawo ndiponso amene salabadira mawu

❮ Previous Next ❯

ترجمة: إن الذين لا يرجون لقاءنا ورضوا بالحياة الدنيا واطمأنوا بها والذين هم, باللغة نيانجا

﴿إن الذين لا يرجون لقاءنا ورضوا بالحياة الدنيا واطمأنوا بها والذين هم﴾ [يُونس: 7]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndithu amene sayembekeza kukumana Nafe, nakondetsetsa umoyo wapadziko lapansi ndi kukhazikika (mtima) ndi za mmenemo, ndi omwe akunyozera Ayah Zathu
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek