×

Zitatha izi, tidatumiza Atumwi ena kwa anthu awo. Iwo adadza kwa iwo 10:74 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Yunus ⮕ (10:74) ayat 74 in Chichewa

10:74 Surah Yunus ayat 74 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Yunus ayat 74 - يُونس - Page - Juz 11

﴿ثُمَّ بَعَثۡنَا مِنۢ بَعۡدِهِۦ رُسُلًا إِلَىٰ قَوۡمِهِمۡ فَجَآءُوهُم بِٱلۡبَيِّنَٰتِ فَمَا كَانُواْ لِيُؤۡمِنُواْ بِمَا كَذَّبُواْ بِهِۦ مِن قَبۡلُۚ كَذَٰلِكَ نَطۡبَعُ عَلَىٰ قُلُوبِ ٱلۡمُعۡتَدِينَ ﴾
[يُونس: 74]

Zitatha izi, tidatumiza Atumwi ena kwa anthu awo. Iwo adadza kwa iwo ndi zizindikiro zooneka koma iwo sanali okhulupirira mzimene adazikana kale. Mmenemo ndi mmene timadindira zidindo mitima ya anthu ochita zinthu mopyora muyeso

❮ Previous Next ❯

ترجمة: ثم بعثنا من بعده رسلا إلى قومهم فجاءوهم بالبينات فما كانوا ليؤمنوا, باللغة نيانجا

﴿ثم بعثنا من بعده رسلا إلى قومهم فجاءوهم بالبينات فما كانوا ليؤمنوا﴾ [يُونس: 74]

Khaled Ibrahim Betala
“Pambuyo pake tidawatumiza atumiki (ambiri) kwa anthu awo. Adawadzera ndi zisonyezo zoonekera poyera koma sadali okhulupirira zimene ena adazitsutsa kale, (adatsatira njira zomwezo za anzawo). Umo ndi momwe tikudindira zidindo m’mitima ya anthu opyola malire
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek