×

Pambuyo pake tinatumiza Mose ndi Aroni ndi zizindikiro zathu kwa Farawo ndi 10:75 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Yunus ⮕ (10:75) ayat 75 in Chichewa

10:75 Surah Yunus ayat 75 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Yunus ayat 75 - يُونس - Page - Juz 11

﴿ثُمَّ بَعَثۡنَا مِنۢ بَعۡدِهِم مُّوسَىٰ وَهَٰرُونَ إِلَىٰ فِرۡعَوۡنَ وَمَلَإِيْهِۦ بِـَٔايَٰتِنَا فَٱسۡتَكۡبَرُواْ وَكَانُواْ قَوۡمٗا مُّجۡرِمِينَ ﴾
[يُونس: 75]

Pambuyo pake tinatumiza Mose ndi Aroni ndi zizindikiro zathu kwa Farawo ndi nduna zake. Koma iwo adadzikweza ndipo anali anthu oipa

❮ Previous Next ❯

ترجمة: ثم بعثنا من بعدهم موسى وهارون إلى فرعون وملئه بآياتنا فاستكبروا وكانوا, باللغة نيانجا

﴿ثم بعثنا من بعدهم موسى وهارون إلى فرعون وملئه بآياتنا فاستكبروا وكانوا﴾ [يُونس: 75]

Khaled Ibrahim Betala
“Kenako pambuyo pawo tidamtuma Mûsa ndi Haarun pamodzi ndi zizindikiro zathu kwa Farawo ndi nduna zake, koma adadzikweza. Tero adali anthu ochita zoipa
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek