×

Iwo adati: “Kodi iwe wadza kuti utitembenuze m’zimene tidapeza makolo athu akuchita 10:78 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Yunus ⮕ (10:78) ayat 78 in Chichewa

10:78 Surah Yunus ayat 78 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Yunus ayat 78 - يُونس - Page - Juz 11

﴿قَالُوٓاْ أَجِئۡتَنَا لِتَلۡفِتَنَا عَمَّا وَجَدۡنَا عَلَيۡهِ ءَابَآءَنَا وَتَكُونَ لَكُمَا ٱلۡكِبۡرِيَآءُ فِي ٱلۡأَرۡضِ وَمَا نَحۡنُ لَكُمَا بِمُؤۡمِنِينَ ﴾
[يُونس: 78]

Iwo adati: “Kodi iwe wadza kuti utitembenuze m’zimene tidapeza makolo athu akuchita ndi cholinga chakuti inu anthu awiri, mukhale akuluakulu m’dziko? Ife sitikukhulupirirani anthu awirinu.”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: قالوا أجئتنا لتلفتنا عما وجدنا عليه آباءنا وتكون لكما الكبرياء في الأرض, باللغة نيانجا

﴿قالوا أجئتنا لتلفتنا عما وجدنا عليه آباءنا وتكون لكما الكبرياء في الأرض﴾ [يُونس: 78]

Khaled Ibrahim Betala
“(Iwo) adati: “Kodi watidzera kuti utichotse ku zimene tidawapeza nazo makolo athu kuti ukulu ukhale wa inu awiri m’dzikoli? Koma ife sitingakukhulupirireni awirinu.”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek