×

Ife tidatsogolera ana a Israyeli kuoloka nyanja. Farawo, pamodzi ndi magulu ake 10:90 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Yunus ⮕ (10:90) ayat 90 in Chichewa

10:90 Surah Yunus ayat 90 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Yunus ayat 90 - يُونس - Page - Juz 11

﴿۞ وَجَٰوَزۡنَا بِبَنِيٓ إِسۡرَٰٓءِيلَ ٱلۡبَحۡرَ فَأَتۡبَعَهُمۡ فِرۡعَوۡنُ وَجُنُودُهُۥ بَغۡيٗا وَعَدۡوًاۖ حَتَّىٰٓ إِذَآ أَدۡرَكَهُ ٱلۡغَرَقُ قَالَ ءَامَنتُ أَنَّهُۥ لَآ إِلَٰهَ إِلَّا ٱلَّذِيٓ ءَامَنَتۡ بِهِۦ بَنُوٓاْ إِسۡرَٰٓءِيلَ وَأَنَا۠ مِنَ ٱلۡمُسۡلِمِينَ ﴾
[يُونس: 90]

Ife tidatsogolera ana a Israyeli kuoloka nyanja. Farawo, pamodzi ndi magulu ake a nkhondo, adawatsatira ndi chiwembu ndiponso udani. Kufikira pamene anali kumira, Farawo adati: “Ndikhulupirira kuti kulibe mulungu koma Iye amene ana a Israyeli amamukhulupirira. Ndipo ine ndili m’modzi wa odzipereka pogonjera.”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: وجاوزنا ببني إسرائيل البحر فأتبعهم فرعون وجنوده بغيا وعدوا حتى إذا أدركه, باللغة نيانجا

﴿وجاوزنا ببني إسرائيل البحر فأتبعهم فرعون وجنوده بغيا وعدوا حتى إذا أدركه﴾ [يُونس: 90]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndipo tidawaolotsa pa nyanja ana a Israyeli. Ndipo Farawo ndi asilikali ake ankhondo adawatsata moipitsa ndi mwamtopola, kufikira pamene kumira kudampeza; (iye) adati: “Ndakhulupirira kuti palibe wopembedzedwa mwachoonadi koma Yemwe ana a Israyeli amkhulupirira. Ndipo ine ndine mmodzi mwa Asilamu (omugonjera monga iwo akumgonjera).”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek