×

Ndipo chita mapemphero ako nthawi ziwiri za masana ndi m’maola oyambirira a 11:114 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Hud ⮕ (11:114) ayat 114 in Chichewa

11:114 Surah Hud ayat 114 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Hud ayat 114 - هُود - Page - Juz 12

﴿وَأَقِمِ ٱلصَّلَوٰةَ طَرَفَيِ ٱلنَّهَارِ وَزُلَفٗا مِّنَ ٱلَّيۡلِۚ إِنَّ ٱلۡحَسَنَٰتِ يُذۡهِبۡنَ ٱلسَّيِّـَٔاتِۚ ذَٰلِكَ ذِكۡرَىٰ لِلذَّٰكِرِينَ ﴾
[هُود: 114]

Ndipo chita mapemphero ako nthawi ziwiri za masana ndi m’maola oyambirira a usiku. Ndithudi ntchito zabwino zimafafaniza machimo. Chimenechi ndi chikumbutso kwa anthu okumbukira

❮ Previous Next ❯

ترجمة: وأقم الصلاة طرفي النهار وزلفا من الليل إن الحسنات يذهبن السيئات ذلك, باللغة نيانجا

﴿وأقم الصلاة طرفي النهار وزلفا من الليل إن الحسنات يذهبن السيئات ذلك﴾ [هُود: 114]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndipo pemphera Swala nsonga ziwiri za usana ndi nthawi za usiku zomwe zili pafupi ndi usana. Ndithu zabwino zimachotsa zoipa. Ichi ndi chikumbutso kwa okumbukira
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek