×

Fanizo la magulu awiri a anthu lili ngati munthu wakhungu ndi wosamva, 11:24 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Hud ⮕ (11:24) ayat 24 in Chichewa

11:24 Surah Hud ayat 24 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Hud ayat 24 - هُود - Page - Juz 12

﴿۞ مَثَلُ ٱلۡفَرِيقَيۡنِ كَٱلۡأَعۡمَىٰ وَٱلۡأَصَمِّ وَٱلۡبَصِيرِ وَٱلسَّمِيعِۚ هَلۡ يَسۡتَوِيَانِ مَثَلًاۚ أَفَلَا تَذَكَّرُونَ ﴾
[هُود: 24]

Fanizo la magulu awiri a anthu lili ngati munthu wakhungu ndi wosamva, wopenya ndi wakumva. Kodi magulu awiriwa ndi ofanana? Kodi simungaganize pamenepa

❮ Previous Next ❯

ترجمة: مثل الفريقين كالأعمى والأصم والبصير والسميع هل يستويان مثلا أفلا تذكرون, باللغة نيانجا

﴿مثل الفريقين كالأعمى والأصم والبصير والسميع هل يستويان مثلا أفلا تذكرون﴾ [هُود: 24]

Khaled Ibrahim Betala
“Fanizo la magulu awiriwa (okhulupirira ndi osakhulupirira), lili ngati (munthu) wakhungu ndi gonthi, ndi (munthu) wopenya ndi wakumva. Kodi awiriwa angakhale ofanana (pa chikhalidwe chawo)? Bwanji simukuganiza
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek