×

Ndithudi iwo amene akhulupirira ndipo amachita ntchito zabwino, ndipo amadzichepetsa kwambiri pamaso 11:23 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Hud ⮕ (11:23) ayat 23 in Chichewa

11:23 Surah Hud ayat 23 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Hud ayat 23 - هُود - Page - Juz 12

﴿إِنَّ ٱلَّذِينَ ءَامَنُواْ وَعَمِلُواْ ٱلصَّٰلِحَٰتِ وَأَخۡبَتُوٓاْ إِلَىٰ رَبِّهِمۡ أُوْلَٰٓئِكَ أَصۡحَٰبُ ٱلۡجَنَّةِۖ هُمۡ فِيهَا خَٰلِدُونَ ﴾
[هُود: 23]

Ndithudi iwo amene akhulupirira ndipo amachita ntchito zabwino, ndipo amadzichepetsa kwambiri pamaso pa Ambuye wawo, iwo adzakhala eni ake a Paradiso ndipo kumeneko adzakhalako mpaka kalekale

❮ Previous Next ❯

ترجمة: إن الذين آمنوا وعملوا الصالحات وأخبتوا إلى ربهم أولئك أصحاب الجنة هم, باللغة نيانجا

﴿إن الذين آمنوا وعملوا الصالحات وأخبتوا إلى ربهم أولئك أصحاب الجنة هم﴾ [هُود: 23]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndithu amene akhulupirira ndi kumachita zabwino ndi kumadzichepetsa kwa Mbuye wawo, iwowo ndiwo anthu a ku Munda wamtendere. M’menemo adzakhala nthawi yaitali
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek