×

Ndipo kudanenedwa: “Nthaka meza madzi ako! Ndi kumwamba siya kugwetsa mvula.” Chigumula 11:44 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Hud ⮕ (11:44) ayat 44 in Chichewa

11:44 Surah Hud ayat 44 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Hud ayat 44 - هُود - Page - Juz 12

﴿وَقِيلَ يَٰٓأَرۡضُ ٱبۡلَعِي مَآءَكِ وَيَٰسَمَآءُ أَقۡلِعِي وَغِيضَ ٱلۡمَآءُ وَقُضِيَ ٱلۡأَمۡرُ وَٱسۡتَوَتۡ عَلَى ٱلۡجُودِيِّۖ وَقِيلَ بُعۡدٗا لِّلۡقَوۡمِ ٱلظَّٰلِمِينَ ﴾
[هُود: 44]

Ndipo kudanenedwa: “Nthaka meza madzi ako! Ndi kumwamba siya kugwetsa mvula.” Chigumula chinasiya ndipo chifuniro cha Mulungu chinakwaniritsidwa. Ndipo chombo chinadzaima pa phiri la Al Judi ndipo panamveka mawu onena kuti: “Chionongeko chili kwa anthu ochita zoipa.”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: وقيل ياأرض ابلعي ماءك وياسماء أقلعي وغيض الماء وقضي الأمر واستوت على, باللغة نيانجا

﴿وقيل ياأرض ابلعي ماءك وياسماء أقلعي وغيض الماء وقضي الأمر واستوت على﴾ [هُود: 44]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndipo (pambuyo poonongeka onse ndi zonse zomwe Allah adafuna kuti zionongeke), kudanenedwa: “E iwe nthaka! Meza madzi ako. Ndipo iwe thambo! Amange (madzi ako amvula).” Choncho, madzi adaphwa ndipo lamulo lidakwaniritsidwa (loononga anthu oipa). Ndipo (chombo) chidaima pamwamba pa (phiri lotchedwa) Judi, ndipo kudanenedwa: “Aonongeke onse ochita zoipa.”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek