×

Ndipo kwa Thamoud, tidatumiza m’bale wawo Saleh. Iye adati: “Oh anthu anga! 11:61 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Hud ⮕ (11:61) ayat 61 in Chichewa

11:61 Surah Hud ayat 61 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Hud ayat 61 - هُود - Page - Juz 12

﴿۞ وَإِلَىٰ ثَمُودَ أَخَاهُمۡ صَٰلِحٗاۚ قَالَ يَٰقَوۡمِ ٱعۡبُدُواْ ٱللَّهَ مَا لَكُم مِّنۡ إِلَٰهٍ غَيۡرُهُۥۖ هُوَ أَنشَأَكُم مِّنَ ٱلۡأَرۡضِ وَٱسۡتَعۡمَرَكُمۡ فِيهَا فَٱسۡتَغۡفِرُوهُ ثُمَّ تُوبُوٓاْ إِلَيۡهِۚ إِنَّ رَبِّي قَرِيبٞ مُّجِيبٞ ﴾
[هُود: 61]

Ndipo kwa Thamoud, tidatumiza m’bale wawo Saleh. Iye adati: “Oh anthu anga! Mpembedzeni Mulungu, chifukwa inu mulibe mulungu wina kupatula Iye yekha. Iye ndiye amene adakulengani inu kuchokera ku nthaka, ndipo adakupatsani inu malo okhala pa nthakayo. Motero funani chikhululukiro kwa Iye ndipo idzani kwa Iye ndi kulapa. Ndithudi Ambuye wanga ali pafupi nanu ndipo Iye adzamva mapemphero anu.”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: وإلى ثمود أخاهم صالحا قال ياقوم اعبدوا الله ما لكم من إله, باللغة نيانجا

﴿وإلى ثمود أخاهم صالحا قال ياقوم اعبدوا الله ما لكم من إله﴾ [هُود: 61]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndipo kwa anthu (a mtundu) wa Samud, (tidatuma) m’bale wawo Swaleh. Adati: “E inu anthu anga! Lambirani Allah. Mulibe mulungu wina koma Iye Yekha. Iye adakuumbani ndi nthaka ndi kukukhazikani m’menemo. Ndipo mpempheni chikhululuko (pa zolakwa zanu), kenako tembenukirani kwa Iye. Ndithu Mbuye wanga ali pafupi (ndi akapolo Ake). Ndipo Ngovomera mapempho (aopempha).”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek