×

Koma iwo adaipha ngamirayo ndipo iye adati: “Inu basangalalani m’nyumba zanu masiku 11:65 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Hud ⮕ (11:65) ayat 65 in Chichewa

11:65 Surah Hud ayat 65 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Hud ayat 65 - هُود - Page - Juz 12

﴿فَعَقَرُوهَا فَقَالَ تَمَتَّعُواْ فِي دَارِكُمۡ ثَلَٰثَةَ أَيَّامٖۖ ذَٰلِكَ وَعۡدٌ غَيۡرُ مَكۡذُوبٖ ﴾
[هُود: 65]

Koma iwo adaipha ngamirayo ndipo iye adati: “Inu basangalalani m’nyumba zanu masiku atatu. Chimenecho ndi chipangano chimene sichili chabodza.”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: فعقروها فقال تمتعوا في داركم ثلاثة أيام ذلك وعد غير مكذوب, باللغة نيانجا

﴿فعقروها فقال تمتعوا في داركم ثلاثة أيام ذلك وعد غير مكذوب﴾ [هُود: 65]

Khaled Ibrahim Betala
“Koma adaipha. Choncho (Swaleh) adati: “Sangalalani m’midzi yanuyi pamasiku atatu. (Kenako mulangidwa). Limenelo ndi lonjezo osati labodza.”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek