×

Ndipo pamene chiweruzo chathu chimadza, Ife tinamupulumutsa Saleh pamodzi ndi amene adakhulupirira 11:66 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Hud ⮕ (11:66) ayat 66 in Chichewa

11:66 Surah Hud ayat 66 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Hud ayat 66 - هُود - Page - Juz 12

﴿فَلَمَّا جَآءَ أَمۡرُنَا نَجَّيۡنَا صَٰلِحٗا وَٱلَّذِينَ ءَامَنُواْ مَعَهُۥ بِرَحۡمَةٖ مِّنَّا وَمِنۡ خِزۡيِ يَوۡمِئِذٍۚ إِنَّ رَبَّكَ هُوَ ٱلۡقَوِيُّ ٱلۡعَزِيزُ ﴾
[هُود: 66]

Ndipo pamene chiweruzo chathu chimadza, Ife tinamupulumutsa Saleh pamodzi ndi amene adakhulupirira ndi iye kudzera m’Chisomo chathu, kuchokera m’masautso a tsiku limeneli. Ndithudi Ambuye wako ndi wanyonga, ndi wopambana

❮ Previous Next ❯

ترجمة: فلما جاء أمرنا نجينا صالحا والذين آمنوا معه برحمة منا ومن خزي, باللغة نيانجا

﴿فلما جاء أمرنا نجينا صالحا والذين آمنوا معه برحمة منا ومن خزي﴾ [هُود: 66]

Khaled Ibrahim Betala
“Choncho pamene lamulo Lathu lidadza (lakuononga midziyo), tidampulumutsa Swalih ndi anthu amene adakhulupirira naye, kukuyaluka kwa tsiku limenelo, mwa chifundo Chathu. Ndithu Mbuye wako ndi Mwini mphamvu, Ngopambana
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek