×

Ndipo pamene chilamulo chathu chidadza, Ife tidatembenuza pamwamba pa Mzinda kukhala pansi 11:82 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Hud ⮕ (11:82) ayat 82 in Chichewa

11:82 Surah Hud ayat 82 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Hud ayat 82 - هُود - Page - Juz 12

﴿فَلَمَّا جَآءَ أَمۡرُنَا جَعَلۡنَا عَٰلِيَهَا سَافِلَهَا وَأَمۡطَرۡنَا عَلَيۡهَا حِجَارَةٗ مِّن سِجِّيلٖ مَّنضُودٖ ﴾
[هُود: 82]

Ndipo pamene chilamulo chathu chidadza, Ife tidatembenuza pamwamba pa Mzinda kukhala pansi ndipo tidagwetsa pa iwo miyala youmbidwa ndi nthaka ya makande younjikika

❮ Previous Next ❯

ترجمة: فلما جاء أمرنا جعلنا عاليها سافلها وأمطرنا عليها حجارة من سجيل منضود, باللغة نيانجا

﴿فلما جاء أمرنا جعلنا عاليها سافلها وأمطرنا عليها حجارة من سجيل منضود﴾ [هُود: 82]

Khaled Ibrahim Betala
“Choncho, pamene lidadza lamulo lathu, tidaugadabula (m’zindawo) kumwamba kukhala pansi, pansi kukhala kumwamba, ndipo tidawavumbwitsira mvula ya sangalawe zopangika ndi dongo lotentheka ndi moto, zogwirana kwambiri
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek