×

Nena, “Iyi ndi njira yanga. Ine mosakayika, ndili kukuitanani ndi nzeru kuti 12:108 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Yusuf ⮕ (12:108) ayat 108 in Chichewa

12:108 Surah Yusuf ayat 108 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Yusuf ayat 108 - يُوسُف - Page - Juz 13

﴿قُلۡ هَٰذِهِۦ سَبِيلِيٓ أَدۡعُوٓاْ إِلَى ٱللَّهِۚ عَلَىٰ بَصِيرَةٍ أَنَا۠ وَمَنِ ٱتَّبَعَنِيۖ وَسُبۡحَٰنَ ٱللَّهِ وَمَآ أَنَا۠ مِنَ ٱلۡمُشۡرِكِينَ ﴾
[يُوسُف: 108]

Nena, “Iyi ndi njira yanga. Ine mosakayika, ndili kukuitanani ndi nzeru kuti mukhale ndi chikhulupiriro mwa Mulungu, ine pamodzi ndi onditsatira anga. Ulemerero ukhale kwa Mulungu ndipo ine sindine wopembedza mafano ayi.”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: قل هذه سبيلي أدعو إلى الله على بصيرة أنا ومن اتبعني وسبحان, باللغة نيانجا

﴿قل هذه سبيلي أدعو إلى الله على بصيرة أنا ومن اتبعني وسبحان﴾ [يُوسُف: 108]

Khaled Ibrahim Betala
“Nena: “Iyi ndi njira yanga. Ndikuitanira kwa Allah mwa nzeru zokwanira, ine ndi omwe akunditsata. Ndithu Allah wapatukana (ndi mbiri zopunguka). Ndipo ine sindili mwa ophatikiza (Allah ndi zinthu zina).”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek