×

“Palibechimene mumapembedza kuonjezera pa Iye, koma mayina chabe amene inu ndi makolo 12:40 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Yusuf ⮕ (12:40) ayat 40 in Chichewa

12:40 Surah Yusuf ayat 40 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Yusuf ayat 40 - يُوسُف - Page - Juz 12

﴿مَا تَعۡبُدُونَ مِن دُونِهِۦٓ إِلَّآ أَسۡمَآءٗ سَمَّيۡتُمُوهَآ أَنتُمۡ وَءَابَآؤُكُم مَّآ أَنزَلَ ٱللَّهُ بِهَا مِن سُلۡطَٰنٍۚ إِنِ ٱلۡحُكۡمُ إِلَّا لِلَّهِ أَمَرَ أَلَّا تَعۡبُدُوٓاْ إِلَّآ إِيَّاهُۚ ذَٰلِكَ ٱلدِّينُ ٱلۡقَيِّمُ وَلَٰكِنَّ أَكۡثَرَ ٱلنَّاسِ لَا يَعۡلَمُونَ ﴾
[يُوسُف: 40]

“Palibechimene mumapembedza kuonjezera pa Iye, koma mayina chabe amene inu ndi makolo anu mudapeka, amene Mulungu sadatumize umboni wa mayinawo. Chiweruzo chili m’manja mwa Mulungu yekha. Iye adakulamulirani kuti inu musamapembedze wina koma Iye yekha. Chimenecho ndicho chipembedzo changwiro, koma anthu ambiri sazindikira.”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: ما تعبدون من دونه إلا أسماء سميتموها أنتم وآباؤكم ما أنـزل الله, باللغة نيانجا

﴿ما تعبدون من دونه إلا أسماء سميتموها أنتم وآباؤكم ما أنـزل الله﴾ [يُوسُف: 40]

Khaled Ibrahim Betala
““Simupembedza china kusiya Iye (Allah) koma ndi maina basi amene inu nokha mudawatcha ndi makolo anu, Allah sadatsitse umboni uliwonse pa zimenezo. Palibe lamulo lina koma ndi la Allah basi. Walamula kuti musampembedze aliyense koma Iye basi. Chimenecho ndicho chipembedzo choongoka, koma anthu ambiri sadziwa (monga inu mulili popembedza mafano).”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek