×

Motero pamene iwo anada nkhawa ndi iye, iwo adakhala paokha ndikunong’onezana. Ndipo 12:80 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Yusuf ⮕ (12:80) ayat 80 in Chichewa

12:80 Surah Yusuf ayat 80 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Yusuf ayat 80 - يُوسُف - Page - Juz 13

﴿فَلَمَّا ٱسۡتَيۡـَٔسُواْ مِنۡهُ خَلَصُواْ نَجِيّٗاۖ قَالَ كَبِيرُهُمۡ أَلَمۡ تَعۡلَمُوٓاْ أَنَّ أَبَاكُمۡ قَدۡ أَخَذَ عَلَيۡكُم مَّوۡثِقٗا مِّنَ ٱللَّهِ وَمِن قَبۡلُ مَا فَرَّطتُمۡ فِي يُوسُفَۖ فَلَنۡ أَبۡرَحَ ٱلۡأَرۡضَ حَتَّىٰ يَأۡذَنَ لِيٓ أَبِيٓ أَوۡ يَحۡكُمَ ٱللَّهُ لِيۖ وَهُوَ خَيۡرُ ٱلۡحَٰكِمِينَ ﴾
[يُوسُف: 80]

Motero pamene iwo anada nkhawa ndi iye, iwo adakhala paokha ndikunong’onezana. Ndipo wamkulu wawo adati, “Kodi inu simudziwa kuti abambo anu adatenga lonjezo kwa inu, M’dzina la Mulungu ndiponso kuti mudaphwanya chikhulupiriro chanu kale ndi nkhani ya Yosefe? Motero ine sindidzachoka m’dziko muno mpaka pamene abambo anga andilola kapena kufikira pamene Mulungu atapereka chiweruzo chake pa nkhani iyi. Iye ndiye Muweruzi wabwino pa aweruzi onse.”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: فلما استيأسوا منه خلصوا نجيا قال كبيرهم ألم تعلموا أن أباكم قد, باللغة نيانجا

﴿فلما استيأسوا منه خلصوا نجيا قال كبيرهم ألم تعلموا أن أباكم قد﴾ [يُوسُف: 80]

Khaled Ibrahim Betala
“Choncho, pamene adataya mtima za iye, adapita pambali kukanong’onezana. Wamkulu wawo adati: “Kodi simudziwa kuti bambo wanu adatenga lonjezo kuchokera kwa inu m’dzina la Allah (kuti mudzam’bweza iyeyo?) ndiponso kale mudalakwa (pa mapangano anu) pa za Yûsuf. Choncho sindichoka dziko lino kufikira atandilola bambo (kutero) kapena Allah andilamule (zondichotsa kuno pomasulidwa m’bale wangayu); Iye Ngwabwino polamula kuposa olamula.”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek