×

“Bwererani kwa atate wanu ndipo mukawauze kuti, “Oh Bambo wathu! Ndithudi mwana 12:81 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Yusuf ⮕ (12:81) ayat 81 in Chichewa

12:81 Surah Yusuf ayat 81 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Yusuf ayat 81 - يُوسُف - Page - Juz 13

﴿ٱرۡجِعُوٓاْ إِلَىٰٓ أَبِيكُمۡ فَقُولُواْ يَٰٓأَبَانَآ إِنَّ ٱبۡنَكَ سَرَقَ وَمَا شَهِدۡنَآ إِلَّا بِمَا عَلِمۡنَا وَمَا كُنَّا لِلۡغَيۡبِ حَٰفِظِينَ ﴾
[يُوسُف: 81]

“Bwererani kwa atate wanu ndipo mukawauze kuti, “Oh Bambo wathu! Ndithudi mwana wanu waba ndipo ife sitiikira umboni kupatula pa zimene tikudziwa. Ndipo ife sitikadadziwa zinthu zobisika!”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: ارجعوا إلى أبيكم فقولوا ياأبانا إن ابنك سرق وما شهدنا إلا بما, باللغة نيانجا

﴿ارجعوا إلى أبيكم فقولوا ياأبانا إن ابنك سرق وما شهدنا إلا بما﴾ [يُوسُف: 81]

Khaled Ibrahim Betala
““Bwererani kwa bambo wanu ndipo mukawauze (kuti): “E bambo wathu! Ndithu mwana wanu waba. Ndipo ife sitidaikire umboni (wakuti wakuba achitidwe ukapolo) koma pa zomwe tidazidziwa (kuti mwa ife mulibe wakuba), ndipo sitidali kudziwa zamseri.”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek