×

Inu mumakhala m’nyumba za anthu amene adachimwira miyoyo yawo pamene mumadziwa zonse 14:45 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Ibrahim ⮕ (14:45) ayat 45 in Chichewa

14:45 Surah Ibrahim ayat 45 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Ibrahim ayat 45 - إبراهِيم - Page - Juz 13

﴿وَسَكَنتُمۡ فِي مَسَٰكِنِ ٱلَّذِينَ ظَلَمُوٓاْ أَنفُسَهُمۡ وَتَبَيَّنَ لَكُمۡ كَيۡفَ فَعَلۡنَا بِهِمۡ وَضَرَبۡنَا لَكُمُ ٱلۡأَمۡثَالَ ﴾
[إبراهِيم: 45]

Inu mumakhala m’nyumba za anthu amene adachimwira miyoyo yawo pamene mumadziwa zonse zimene tidawachitira iwo. Ndipo Ife tidakuikirani chitsanzo

❮ Previous Next ❯

ترجمة: وسكنتم في مساكن الذين ظلموا أنفسهم وتبين لكم كيف فعلنا بهم وضربنا, باللغة نيانجا

﴿وسكنتم في مساكن الذين ظلموا أنفسهم وتبين لكم كيف فعلنا بهم وضربنا﴾ [إبراهِيم: 45]

Khaled Ibrahim Betala
““Chikhalirecho mudakhala m’malo mommuja mwa omwe adadzichitira okha zoipa; ndipo kudaonekeratu poyera kwa inu mmene tidawachitira (powaononga); ndipo tidakufotokozerani mafanizo (osiyanasiyana koma inu mudatsutsa).”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek