×

Ena a iwo adati, Adali atatu ndipo galu wawo adali wachinayi, pamene 18:22 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-Kahf ⮕ (18:22) ayat 22 in Chichewa

18:22 Surah Al-Kahf ayat 22 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-Kahf ayat 22 - الكَهف - Page - Juz 15

﴿سَيَقُولُونَ ثَلَٰثَةٞ رَّابِعُهُمۡ كَلۡبُهُمۡ وَيَقُولُونَ خَمۡسَةٞ سَادِسُهُمۡ كَلۡبُهُمۡ رَجۡمَۢا بِٱلۡغَيۡبِۖ وَيَقُولُونَ سَبۡعَةٞ وَثَامِنُهُمۡ كَلۡبُهُمۡۚ قُل رَّبِّيٓ أَعۡلَمُ بِعِدَّتِهِم مَّا يَعۡلَمُهُمۡ إِلَّا قَلِيلٞۗ فَلَا تُمَارِ فِيهِمۡ إِلَّا مِرَآءٗ ظَٰهِرٗا وَلَا تَسۡتَفۡتِ فِيهِم مِّنۡهُمۡ أَحَدٗا ﴾
[الكَهف: 22]

Ena a iwo adati, Adali atatu ndipo galu wawo adali wachinayi, pamene ena akuti adali asanu ndipo galu wawo adali wachisanu ndi chimodzi. Moganizira zinthu zobisika, ena akuti adalipo asanu ndi awiri ndipo galu wawo adali wachisanu ndi chitatu. Nena, “Ambuye wanga ndi wodziwa kwambiri chiwerengero chawo, palibe amene akuwadziwa kupatula ochepa okha.” Usakangane nawo za iwo kupatula mkangano womveka. Ndipo usamufunse wina aliyense wa anthu zokhudza anthu a kuphanga

❮ Previous Next ❯

ترجمة: سيقولون ثلاثة رابعهم كلبهم ويقولون خمسة سادسهم كلبهم رجما بالغيب ويقولون سبعة, باللغة نيانجا

﴿سيقولون ثلاثة رابعهم كلبهم ويقولون خمسة سادسهم كلبهم رجما بالغيب ويقولون سبعة﴾ [الكَهف: 22]

Khaled Ibrahim Betala
“(Ena) akhala akunena (kuti) adali anthu atatu, wachinayi ndi galu wawo; ndipo (ena) akuti adali asanu, wachisanu ndichimodzi ndigalu wawo. (Akunena) mwakungoganizira chabe zomwe sakuzidziwa; ndipo (ena) akuti adali asanu ndi awiri, ndipo wachisanu ndi chitatu ndi galu wawo. Nena: “Mbuye wanga ndiye akudziwa bwinobwino za chiwerengero chawo. Palibe amene akudziwa (za iwo) koma ndi ochepa chabe.” Choncho usatsutsane nawo za iwo, kupatula kutsutsana kwa pa zinthu zodziwika, ndipo usamfunse aliyense mwa iwo za iwo
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek