×

Pa tsiku limeneli, anthu adzatsatira woitana wa Mulungu, mopanda chinyengo. Ndipo mawu 20:108 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Ta-Ha ⮕ (20:108) ayat 108 in Chichewa

20:108 Surah Ta-Ha ayat 108 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Ta-Ha ayat 108 - طه - Page - Juz 16

﴿يَوۡمَئِذٖ يَتَّبِعُونَ ٱلدَّاعِيَ لَا عِوَجَ لَهُۥۖ وَخَشَعَتِ ٱلۡأَصۡوَاتُ لِلرَّحۡمَٰنِ فَلَا تَسۡمَعُ إِلَّا هَمۡسٗا ﴾
[طه: 108]

Pa tsiku limeneli, anthu adzatsatira woitana wa Mulungu, mopanda chinyengo. Ndipo mawu onse adzachepetsedwa chifukwa cha Mwini chisoni ndipo iwe siudzamva china kupatula mgugu wochepa wa mapazi awo

❮ Previous Next ❯

ترجمة: يومئذ يتبعون الداعي لا عوج له وخشعت الأصوات للرحمن فلا تسمع إلا, باللغة نيانجا

﴿يومئذ يتبعون الداعي لا عوج له وخشعت الأصوات للرحمن فلا تسمع إلا﴾ [طه: 108]

Khaled Ibrahim Betala
“Tsiku limenelo adzamtsatira woitana; sadzatha kumpatuka, ndipo mawu (azolengedwa) adzatonthola (kuti chete) kwa (Allah) Wachifundo chambiri; ndipo sudzamva, koma kunong’ona basi (ndi mididi ya mapazi)
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek