×

Mulungu adzati, “Chifukwa chakuti pamene chivumbulutso chathu chinadza kwa iwe udachiiwala. Chimodzimodzi 20:126 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Ta-Ha ⮕ (20:126) ayat 126 in Chichewa

20:126 Surah Ta-Ha ayat 126 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Ta-Ha ayat 126 - طه - Page - Juz 16

﴿قَالَ كَذَٰلِكَ أَتَتۡكَ ءَايَٰتُنَا فَنَسِيتَهَاۖ وَكَذَٰلِكَ ٱلۡيَوۡمَ تُنسَىٰ ﴾
[طه: 126]

Mulungu adzati, “Chifukwa chakuti pamene chivumbulutso chathu chinadza kwa iwe udachiiwala. Chimodzimodzi tsiku lino nawenso waiwalidwa.”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: قال كذلك أتتك آياتنا فنسيتها وكذلك اليوم تنسى, باللغة نيانجا

﴿قال كذلك أتتك آياتنا فنسيتها وكذلك اليوم تنسى﴾ [طه: 126]

Khaled Ibrahim Betala
“(Allah) adzanena: “Zimenezo nchifukwa chakuti zidakudzera Ayah zathu koma udaziiwala (chifukwa chosalabadira), momwemo lero uiwalidwa, (salabadilidwa).”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek