×

Kodi iwo saona mibadwo ya anthu imene tidaiononga iwo asanadze? Iwo amayenda 20:128 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Ta-Ha ⮕ (20:128) ayat 128 in Chichewa

20:128 Surah Ta-Ha ayat 128 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Ta-Ha ayat 128 - طه - Page - Juz 16

﴿أَفَلَمۡ يَهۡدِ لَهُمۡ كَمۡ أَهۡلَكۡنَا قَبۡلَهُم مِّنَ ٱلۡقُرُونِ يَمۡشُونَ فِي مَسَٰكِنِهِمۡۚ إِنَّ فِي ذَٰلِكَ لَأٓيَٰتٖ لِّأُوْلِي ٱلنُّهَىٰ ﴾
[طه: 128]

Kodi iwo saona mibadwo ya anthu imene tidaiononga iwo asanadze? Iwo amayenda pakati pa nyumba zimene iwo anali kukhalamo. Ndithudi mu zimenezi muli zizindikiro kwa anthu a nzeru

❮ Previous Next ❯

ترجمة: أفلم يهد لهم كم أهلكنا قبلهم من القرون يمشون في مساكنهم إن, باللغة نيانجا

﴿أفلم يهد لهم كم أهلكنا قبلهم من القرون يمشون في مساكنهم إن﴾ [طه: 128]

Khaled Ibrahim Betala
“Kodi sizidadziwikebe kwa iwo kuti ndi mibadwo ingati tidaiononga patsogolo pawo? Ndipo awa (osakhulupirira atsopano) akuyenda m’malo awo, (kodi saona zizindikiro zakuonongeka kwawo)? Ndithu m’zimenezo muli zisonyezo kwa eni nzeru
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek