×

Mose adabwerera kwa anthu ake ndi mkwiyo ndiponso mwachisoni. Iye adati, “Anthu 20:86 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Ta-Ha ⮕ (20:86) ayat 86 in Chichewa

20:86 Surah Ta-Ha ayat 86 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Ta-Ha ayat 86 - طه - Page - Juz 16

﴿فَرَجَعَ مُوسَىٰٓ إِلَىٰ قَوۡمِهِۦ غَضۡبَٰنَ أَسِفٗاۚ قَالَ يَٰقَوۡمِ أَلَمۡ يَعِدۡكُمۡ رَبُّكُمۡ وَعۡدًا حَسَنًاۚ أَفَطَالَ عَلَيۡكُمُ ٱلۡعَهۡدُ أَمۡ أَرَدتُّمۡ أَن يَحِلَّ عَلَيۡكُمۡ غَضَبٞ مِّن رَّبِّكُمۡ فَأَخۡلَفۡتُم مَّوۡعِدِي ﴾
[طه: 86]

Mose adabwerera kwa anthu ake ndi mkwiyo ndiponso mwachisoni. Iye adati, “Anthu anga! Kodi Ambuye wanu sadakulonjezeni lonjezo labwino? Kodi munaona nthawi ya lonjezo kutalika? Kapena chinali cholinga chanu kuti mkwiyo wa Ambuye wanu udze pa inu ndipo inu muphwanye lonjezo lanu kwa ine?”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: فرجع موسى إلى قومه غضبان أسفا قال ياقوم ألم يعدكم ربكم وعدا, باللغة نيانجا

﴿فرجع موسى إلى قومه غضبان أسفا قال ياقوم ألم يعدكم ربكم وعدا﴾ [طه: 86]

Khaled Ibrahim Betala
“Mûsa adabwerera kwa anthu ake ali wokwiya ndi wodandaula. Adati: “E inu anthu anga! Kodi Mbuye wanu sadakulonjezeni lonjezo labwino? Kapena nyengo yalonjezolo idatalika kwa inu? Kapena mudafuna kuti mkwiyo ukutsikireni kuchokera kwa Mbuye wanu; tero mwaswa lonjezo langa”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek