×

Kodi iwe siudaone kuti zinthu zonse zimalambira Mulungu mwachitsanzo zinthu zimene zimakhala 22:18 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-hajj ⮕ (22:18) ayat 18 in Chichewa

22:18 Surah Al-hajj ayat 18 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-hajj ayat 18 - الحج - Page - Juz 17

﴿أَلَمۡ تَرَ أَنَّ ٱللَّهَ يَسۡجُدُۤ لَهُۥۤ مَن فِي ٱلسَّمَٰوَٰتِ وَمَن فِي ٱلۡأَرۡضِ وَٱلشَّمۡسُ وَٱلۡقَمَرُ وَٱلنُّجُومُ وَٱلۡجِبَالُ وَٱلشَّجَرُ وَٱلدَّوَآبُّ وَكَثِيرٞ مِّنَ ٱلنَّاسِۖ وَكَثِيرٌ حَقَّ عَلَيۡهِ ٱلۡعَذَابُۗ وَمَن يُهِنِ ٱللَّهُ فَمَا لَهُۥ مِن مُّكۡرِمٍۚ إِنَّ ٱللَّهَ يَفۡعَلُ مَا يَشَآءُ۩ ﴾
[الحج: 18]

Kodi iwe siudaone kuti zinthu zonse zimalambira Mulungu mwachitsanzo zinthu zimene zimakhala kumwamba ndi padziko lapansi monga dzuwa, mwezi, nyenyezi, mapiri mitengo, nyama ndi anthu ambiri? Koma pali ambiri amene chilango ndi chowayenera. Aliyense amene achititsidwa manyazi ndi Mulungu, palibe wina amene angamulemekeze. Ndithudi! Mulungu amachita zimene afuna

❮ Previous Next ❯

ترجمة: ألم تر أن الله يسجد له من في السموات ومن في الأرض, باللغة نيانجا

﴿ألم تر أن الله يسجد له من في السموات ومن في الأرض﴾ [الحج: 18]

❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek