×

Anthuwo ndi amene apirikitsidwa kuchokerakunyumbazawomopandachilungamochifukwa chakuti iwo anati, “Ambuye wathu ndi Mulungu.” 22:40 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-hajj ⮕ (22:40) ayat 40 in Chichewa

22:40 Surah Al-hajj ayat 40 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-hajj ayat 40 - الحج - Page - Juz 17

﴿ٱلَّذِينَ أُخۡرِجُواْ مِن دِيَٰرِهِم بِغَيۡرِ حَقٍّ إِلَّآ أَن يَقُولُواْ رَبُّنَا ٱللَّهُۗ وَلَوۡلَا دَفۡعُ ٱللَّهِ ٱلنَّاسَ بَعۡضَهُم بِبَعۡضٖ لَّهُدِّمَتۡ صَوَٰمِعُ وَبِيَعٞ وَصَلَوَٰتٞ وَمَسَٰجِدُ يُذۡكَرُ فِيهَا ٱسۡمُ ٱللَّهِ كَثِيرٗاۗ وَلَيَنصُرَنَّ ٱللَّهُ مَن يَنصُرُهُۥٓۚ إِنَّ ٱللَّهَ لَقَوِيٌّ عَزِيزٌ ﴾
[الحج: 40]

Anthuwo ndi amene apirikitsidwa kuchokerakunyumbazawomopandachilungamochifukwa chakuti iwo anati, “Ambuye wathu ndi Mulungu.” Ndipo Mulungu akadapanda kuyesa anthu ena ndi mphamvu za anthu anzawo makachisi, matchalitchi, masunagoge ndi mizikiti imene dzina la Mulungu limatchulidwa kwambiri ikadaonongekeratu. Ndithudi Mulungu adzathandiza amene amathandiza chipembedzo chake. Ndithudi Mulungu ndi mphamvu ndiponso Wopambana kwambiri

❮ Previous Next ❯

ترجمة: الذين أخرجوا من ديارهم بغير حق إلا أن يقولوا ربنا الله ولولا, باللغة نيانجا

﴿الذين أخرجوا من ديارهم بغير حق إلا أن يقولوا ربنا الله ولولا﴾ [الحج: 40]

Khaled Ibrahim Betala
“Omwe atulutsidwa m’nyumba zawo popanda chilungamo, koma pachifukwa chakuti akunena: “Mbuye wathu ndi Allah.” Ndipo pakapanda Allah kukankha anthu ena kupyolera mwa ena, (popatsa ena mphamvu kuti agonjetse ena), ndiye kuti Masinagogi, Matchalitchi, nyumba zina zopempheleramo ndi Misikiti momwe dzina la Allah likutchulidwa mochuluka zikadagumulidwa. Ndithu Allah am’thangata amene akuthangata chipembedzo Chake; ndithu Allah Ngwanyonga, Wogonjetsa chilichonse
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek