×

Iwo amene tawapatsa mphamvu padziko lapansi adzapitiriza mapemphero nthawi zonse ndi kupereka 22:41 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-hajj ⮕ (22:41) ayat 41 in Chichewa

22:41 Surah Al-hajj ayat 41 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-hajj ayat 41 - الحج - Page - Juz 17

﴿ٱلَّذِينَ إِن مَّكَّنَّٰهُمۡ فِي ٱلۡأَرۡضِ أَقَامُواْ ٱلصَّلَوٰةَ وَءَاتَوُاْ ٱلزَّكَوٰةَ وَأَمَرُواْ بِٱلۡمَعۡرُوفِ وَنَهَوۡاْ عَنِ ٱلۡمُنكَرِۗ وَلِلَّهِ عَٰقِبَةُ ٱلۡأُمُورِ ﴾
[الحج: 41]

Iwo amene tawapatsa mphamvu padziko lapansi adzapitiriza mapemphero nthawi zonse ndi kupereka msonkho wothandiza osauka, ndipo adzakhazikitsa chilungamo ndi kuletsa zoipa. Kwa Mulungu ndiko kuli mapeto a zinthu zonse

❮ Previous Next ❯

ترجمة: الذين إن مكناهم في الأرض أقاموا الصلاة وآتوا الزكاة وأمروا بالمعروف ونهوا, باللغة نيانجا

﴿الذين إن مكناهم في الأرض أقاموا الصلاة وآتوا الزكاة وأمروا بالمعروف ونهوا﴾ [الحج: 41]

Khaled Ibrahim Betala
“Omwe akuti tikawakhazika pa dziko mwa ubwino, amachita mapemphero a Swala moyenera ndi kupereka Zakaat, ndi kulamula zabwino ndi kuletsa zoipa; ndipo mabwelero a zinthu nkwa Allah basi
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek