×

Chilango chathu chidawapeza mwachilungamo ndipo tidawafafaniza monga zinyalala. Chionongeko kwa anthu onse 23:41 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-Mu’minun ⮕ (23:41) ayat 41 in Chichewa

23:41 Surah Al-Mu’minun ayat 41 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-Mu’minun ayat 41 - المؤمنُون - Page - Juz 18

﴿فَأَخَذَتۡهُمُ ٱلصَّيۡحَةُ بِٱلۡحَقِّ فَجَعَلۡنَٰهُمۡ غُثَآءٗۚ فَبُعۡدٗا لِّلۡقَوۡمِ ٱلظَّٰلِمِينَ ﴾
[المؤمنُون: 41]

Chilango chathu chidawapeza mwachilungamo ndipo tidawafafaniza monga zinyalala. Chionongeko kwa anthu onse ochimwa

❮ Previous Next ❯

ترجمة: فأخذتهم الصيحة بالحق فجعلناهم غثاء فبعدا للقوم الظالمين, باللغة نيانجا

﴿فأخذتهم الصيحة بالحق فجعلناهم غثاء فبعدا للقوم الظالمين﴾ [المؤمنُون: 41]

Khaled Ibrahim Betala
“Choncho, mkuwe wa (chilango) choonadi udawaononga, ndipo tidawachita ngati zinyalala (zongotengedwa ndi madzi). Choncho, kuonongeka kudatsimikizika pa anthu osalungama
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek