×

Kapena monga mdima wa m’nyanja yozama kwambiri yokutidwa ndi mafunde aakulu oyenda 24:40 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah An-Nur ⮕ (24:40) ayat 40 in Chichewa

24:40 Surah An-Nur ayat 40 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah An-Nur ayat 40 - النور - Page - Juz 18

﴿أَوۡ كَظُلُمَٰتٖ فِي بَحۡرٖ لُّجِّيّٖ يَغۡشَىٰهُ مَوۡجٞ مِّن فَوۡقِهِۦ مَوۡجٞ مِّن فَوۡقِهِۦ سَحَابٞۚ ظُلُمَٰتُۢ بَعۡضُهَا فَوۡقَ بَعۡضٍ إِذَآ أَخۡرَجَ يَدَهُۥ لَمۡ يَكَدۡ يَرَىٰهَاۗ وَمَن لَّمۡ يَجۡعَلِ ٱللَّهُ لَهُۥ نُورٗا فَمَا لَهُۥ مِن نُّورٍ ﴾
[النور: 40]

Kapena monga mdima wa m’nyanja yozama kwambiri yokutidwa ndi mafunde aakulu oyenda pamwamba pa mafunde anzake ndi mitambo pamwamba pake ndiponso mdima wosanjana ndi mdima unzake. Ndipo ngati iye atambasula dzanja lake sangathe kuliona. Ndithudi munthu amene saunikidwa ndi Mulungu sangathe kuona kuwala kwa mtundu wina uliwonse

❮ Previous Next ❯

ترجمة: أو كظلمات في بحر لجي يغشاه موج من فوقه موج من فوقه, باللغة نيانجا

﴿أو كظلمات في بحر لجي يغشاه موج من فوقه موج من فوقه﴾ [النور: 40]

Khaled Ibrahim Betala
“Kapena (ntchito zawo zoipazo) zili ngati m’dima mkati mwa nyanja yamadzi ochuluka yomwe yaphimbidwa ndi mafunde, ndipo pamwamba pa mafundewo pali mafundenso. Ndiponso pamwamba pake (mafundewo) pali mitambo. M’dima uwu pamwamba pa m’dima uwu. Akatulutsa mkono wake, sangathe kuuona (chifukwa cha kuchindikala kwa m’dima). Ndipo amene Allah sadampatse kuunika, sakhala nako kuunika
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek