×

Kodi iwe siunaone kuti zonse zimene zili kumwamba ndi pa dziko la 24:41 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah An-Nur ⮕ (24:41) ayat 41 in Chichewa

24:41 Surah An-Nur ayat 41 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah An-Nur ayat 41 - النور - Page - Juz 18

﴿أَلَمۡ تَرَ أَنَّ ٱللَّهَ يُسَبِّحُ لَهُۥ مَن فِي ٱلسَّمَٰوَٰتِ وَٱلۡأَرۡضِ وَٱلطَّيۡرُ صَٰٓفَّٰتٖۖ كُلّٞ قَدۡ عَلِمَ صَلَاتَهُۥ وَتَسۡبِيحَهُۥۗ وَٱللَّهُ عَلِيمُۢ بِمَا يَفۡعَلُونَ ﴾
[النور: 41]

Kodi iwe siunaone kuti zonse zimene zili kumwamba ndi pa dziko la pansi zimalemekeza Mulungu ndiponso pamene mbalame zikutambasula mapiko ake? Chilichonse chimadziwa mapemphero ndi mayamiko omupatsa Iye ndipo Mulungu amadziwa ntchito zawo zonse

❮ Previous Next ❯

ترجمة: ألم تر أن الله يسبح له من في السموات والأرض والطير صافات, باللغة نيانجا

﴿ألم تر أن الله يسبح له من في السموات والأرض والطير صافات﴾ [النور: 41]

Khaled Ibrahim Betala
“Kodi suona kuti zonse zopezeka kumwamba ndi pansi zikumulemekeza Allah, kudzanso mbalame zikatambasula mapiko ake (ngakhalenso zikapanda kutambasula). Chilichonse (mwa zimenezo) chikudziwa pemphero lake ndi m’mene chingamulemekezere (Mlengi wake). Ndipo Allah Ngodziwa zonse zimene akuchita
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek