×

Akakhala anthu osakhulupirira, ntchito zawo zili ngati chizirezire cha m’chipululu. Wapaulendo amene 24:39 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah An-Nur ⮕ (24:39) ayat 39 in Chichewa

24:39 Surah An-Nur ayat 39 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah An-Nur ayat 39 - النور - Page - Juz 18

﴿وَٱلَّذِينَ كَفَرُوٓاْ أَعۡمَٰلُهُمۡ كَسَرَابِۭ بِقِيعَةٖ يَحۡسَبُهُ ٱلظَّمۡـَٔانُ مَآءً حَتَّىٰٓ إِذَا جَآءَهُۥ لَمۡ يَجِدۡهُ شَيۡـٔٗا وَوَجَدَ ٱللَّهَ عِندَهُۥ فَوَفَّىٰهُ حِسَابَهُۥۗ وَٱللَّهُ سَرِيعُ ٱلۡحِسَابِ ﴾
[النور: 39]

Akakhala anthu osakhulupirira, ntchito zawo zili ngati chizirezire cha m’chipululu. Wapaulendo amene ali ndi ludzu amaganiza kuti ndi madzi koma akachiyandikira amaona kuti palibe chilichonse. Iye amamupeza Mulungu pomwepo amene amamupatsa molingana ndi ntchito zake. Mulungu amachita chiwerengero cha zinthu mofulumira

❮ Previous Next ❯

ترجمة: والذين كفروا أعمالهم كسراب بقيعة يحسبه الظمآن ماء حتى إذا جاءه لم, باللغة نيانجا

﴿والذين كفروا أعمالهم كسراب بقيعة يحسبه الظمآن ماء حتى إذا جاءه لم﴾ [النور: 39]

❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek