×

Kodi m’mitima mwawo muli matenda kapena ali ndi chikayiko? Kapena iwo amaopa 24:50 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah An-Nur ⮕ (24:50) ayat 50 in Chichewa

24:50 Surah An-Nur ayat 50 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah An-Nur ayat 50 - النور - Page - Juz 18

﴿أَفِي قُلُوبِهِم مَّرَضٌ أَمِ ٱرۡتَابُوٓاْ أَمۡ يَخَافُونَ أَن يَحِيفَ ٱللَّهُ عَلَيۡهِمۡ وَرَسُولُهُۥۚ بَلۡ أُوْلَٰٓئِكَ هُمُ ٱلظَّٰلِمُونَ ﴾
[النور: 50]

Kodi m’mitima mwawo muli matenda kapena ali ndi chikayiko? Kapena iwo amaopa kuti Mulungu ndi Mtumwi wake akhoza kuwakaniza chiweruzo cholungama? Koma oterewa ndi ochita zoipa

❮ Previous Next ❯

ترجمة: أفي قلوبهم مرض أم ارتابوا أم يخافون أن يحيف الله عليهم ورسوله, باللغة نيانجا

﴿أفي قلوبهم مرض أم ارتابوا أم يخافون أن يحيف الله عليهم ورسوله﴾ [النور: 50]

Khaled Ibrahim Betala
“Kodi ali ndi matenda m’mitima mwawo? Kapena akukaika, kapena akuopa kuti Allah ndi Mtumiki Wake awachitira chinyengo? Koma iwo ndi amene ali osalungama
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek