×

Ndipo pamene adafika pa chitsime cha ku Midiyani, iye adapeza gulu la 28:23 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-Qasas ⮕ (28:23) ayat 23 in Chichewa

28:23 Surah Al-Qasas ayat 23 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-Qasas ayat 23 - القَصَص - Page - Juz 20

﴿وَلَمَّا وَرَدَ مَآءَ مَدۡيَنَ وَجَدَ عَلَيۡهِ أُمَّةٗ مِّنَ ٱلنَّاسِ يَسۡقُونَ وَوَجَدَ مِن دُونِهِمُ ٱمۡرَأَتَيۡنِ تَذُودَانِۖ قَالَ مَا خَطۡبُكُمَاۖ قَالَتَا لَا نَسۡقِي حَتَّىٰ يُصۡدِرَ ٱلرِّعَآءُۖ وَأَبُونَا شَيۡخٞ كَبِيرٞ ﴾
[القَصَص: 23]

Ndipo pamene adafika pa chitsime cha ku Midiyani, iye adapeza gulu la anthu aamuna amene adali kumwetsa ziweto zawo. Ndipo kuonjezera paiwo, padali akazi awiri amene anali kungosunga nkhosa zawo. Mose adati, “Kodi vuto lanu ndi chiyani?” Iwo adati, “Sitingathe kumwetsa nkhosa zathu pokhapokha abusa awa atachotsa ziweto zawo. Ndipo bambo wathu ndi munthu wokalamba.”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: ولما ورد ماء مدين وجد عليه أمة من الناس يسقون ووجد من, باللغة نيانجا

﴿ولما ورد ماء مدين وجد عليه أمة من الناس يسقون ووجد من﴾ [القَصَص: 23]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndipo pamene adawafika madzi a ku Madiyan (pomwe anthu kumeneko ankatungapo madzi), adapeza gulu la anthu likumwetsa (ziweto zawo), ndipo pambali (pa gululo) adapeza akazi awiri akuletsa (ziweto zawo kuti zisapite kukamwa ndi ziweto zinazo). (Mûsa) adati: “Kodi mwatani? (Bwanji simukuzimwetsa ziweto zanu?)” Iwo Adati: “Sitingamwetse (ziweto zathu) mpaka abusa atachotsa (ziweto zawo, chifukwa sitingathe kulimbana nawo). Ndipo bambo wathu ndinkhalamba yaikulu kwabasi.”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek