×

Ngati iwo akanika kukuyankha, dziwa kuti iwo ali kutsatira zilakolako zawo. Kodi 28:50 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-Qasas ⮕ (28:50) ayat 50 in Chichewa

28:50 Surah Al-Qasas ayat 50 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-Qasas ayat 50 - القَصَص - Page - Juz 20

﴿فَإِن لَّمۡ يَسۡتَجِيبُواْ لَكَ فَٱعۡلَمۡ أَنَّمَا يَتَّبِعُونَ أَهۡوَآءَهُمۡۚ وَمَنۡ أَضَلُّ مِمَّنِ ٱتَّبَعَ هَوَىٰهُ بِغَيۡرِ هُدٗى مِّنَ ٱللَّهِۚ إِنَّ ٱللَّهَ لَا يَهۡدِي ٱلۡقَوۡمَ ٱلظَّٰلِمِينَ ﴾
[القَصَص: 50]

Ngati iwo akanika kukuyankha, dziwa kuti iwo ali kutsatira zilakolako zawo. Kodi ndani amene ali wolakwa kwambiri kuposa munthu amene amatsatira zilakolako zake opanda langizo la Mulungu? Ndithudi Mulungu satsogolera anthu olakwa

❮ Previous Next ❯

ترجمة: فإن لم يستجيبوا لك فاعلم أنما يتبعون أهواءهم ومن أضل ممن اتبع, باللغة نيانجا

﴿فإن لم يستجيبوا لك فاعلم أنما يتبعون أهواءهم ومن أضل ممن اتبع﴾ [القَصَص: 50]

Khaled Ibrahim Betala
“Koma ngati sadakuyankhe, dziwa kuti akutsatira zilakolako zawo. Kodi ndani wasokera kwambiri kuposa yemwe akutsatira zilakolako zake popanda chiongoko chochokera kwa Allah? Ndithu Allah saongola anthu odzichitira zoipa
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek