×

Iwo amati, “Ngati ife titsatira chilangizo chako, ife tikuopakulandidwadzikolathu.”KodiIfesitidawakhazikire malo otetezedwa kumene 28:57 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-Qasas ⮕ (28:57) ayat 57 in Chichewa

28:57 Surah Al-Qasas ayat 57 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-Qasas ayat 57 - القَصَص - Page - Juz 20

﴿وَقَالُوٓاْ إِن نَّتَّبِعِ ٱلۡهُدَىٰ مَعَكَ نُتَخَطَّفۡ مِنۡ أَرۡضِنَآۚ أَوَلَمۡ نُمَكِّن لَّهُمۡ حَرَمًا ءَامِنٗا يُجۡبَىٰٓ إِلَيۡهِ ثَمَرَٰتُ كُلِّ شَيۡءٖ رِّزۡقٗا مِّن لَّدُنَّا وَلَٰكِنَّ أَكۡثَرَهُمۡ لَا يَعۡلَمُونَ ﴾
[القَصَص: 57]

Iwo amati, “Ngati ife titsatira chilangizo chako, ife tikuopakulandidwadzikolathu.”KodiIfesitidawakhazikire malo otetezedwa kumene zipatso za mtundu uliwonse zimaperekedwa ngati chakudya kuchokera kwa Ife? Ndithudi ambiri a iwo ndi anthu osadziwa

❮ Previous Next ❯

ترجمة: وقالوا إن نتبع الهدى معك نتخطف من أرضنا أو لم نمكن لهم, باللغة نيانجا

﴿وقالوا إن نتبع الهدى معك نتخطف من أرضنا أو لم نمكن لهم﴾ [القَصَص: 57]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndipo akunena (akafiri a m’ Makka, kuuza Mtumiki): “Ngati titsatira chiongoko (ichi chimene wadza nacho) pamodzi ndi iwe, tifwambidwa m’dziko lathu (potimenya nkhondo mafuko ena a Arabu).” Kodi sitidawakhazike pamalo opatulika ndi pa mtendere pomwe zipatso za mitundumitundu zikudza pamenepo mwaulere (monga rizq) zochokera kwa Ife? Koma ambiri a iwo sadziwa
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek