×

Inu ndinu anthu abwino amene adalengedwera mtundu wa anthu, inu mumalamulira kuchita 3:110 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah al-‘Imran ⮕ (3:110) ayat 110 in Chichewa

3:110 Surah al-‘Imran ayat 110 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah al-‘Imran ayat 110 - آل عِمران - Page - Juz 4

﴿كُنتُمۡ خَيۡرَ أُمَّةٍ أُخۡرِجَتۡ لِلنَّاسِ تَأۡمُرُونَ بِٱلۡمَعۡرُوفِ وَتَنۡهَوۡنَ عَنِ ٱلۡمُنكَرِ وَتُؤۡمِنُونَ بِٱللَّهِۗ وَلَوۡ ءَامَنَ أَهۡلُ ٱلۡكِتَٰبِ لَكَانَ خَيۡرٗا لَّهُمۚ مِّنۡهُمُ ٱلۡمُؤۡمِنُونَ وَأَكۡثَرُهُمُ ٱلۡفَٰسِقُونَ ﴾
[آل عِمران: 110]

Inu ndinu anthu abwino amene adalengedwera mtundu wa anthu, inu mumalamulira kuchita zabwino ndi kuletsa zoipa ndipo mumakhulupilira mwa Mulungu. Ndipo anthu a m’Buku akadakhulupilira, zikadawakhalira bwino. Pakati pawo pali ena amene ali ndi chikhulupiliro, koma ambiri a iwo ndi ochita zoipa

❮ Previous Next ❯

ترجمة: كنتم خير أمة أخرجت للناس تأمرون بالمعروف وتنهون عن المنكر وتؤمنون بالله, باللغة نيانجا

﴿كنتم خير أمة أخرجت للناس تأمرون بالمعروف وتنهون عن المنكر وتؤمنون بالله﴾ [آل عِمران: 110]

Khaled Ibrahim Betala
“Inu (Asilamu) ndinu gulu labwino limene lasankhidwa kwa anthu. Mukulamula (kuchita) zabwino ndi kuletsa zoipa, ndipo mukukhulupirira mwa Allah. Ndipo aja adapatsidwa buku akadakhulupirira monga momwe (adawalamulira) kukadakhala kwabwino kwa iwo. (Koma) mwa iwo alipo okhulupirira pomwe ambiri mwa iwo ngopandukira (chilamulo cha Allah)
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek