×

“Inde, ngati inu mupirira ndi kukhala angwiro ndipo pamene mdani adza mofulumira 3:125 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah al-‘Imran ⮕ (3:125) ayat 125 in Chichewa

3:125 Surah al-‘Imran ayat 125 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah al-‘Imran ayat 125 - آل عِمران - Page - Juz 4

﴿بَلَىٰٓۚ إِن تَصۡبِرُواْ وَتَتَّقُواْ وَيَأۡتُوكُم مِّن فَوۡرِهِمۡ هَٰذَا يُمۡدِدۡكُمۡ رَبُّكُم بِخَمۡسَةِ ءَالَٰفٖ مِّنَ ٱلۡمَلَٰٓئِكَةِ مُسَوِّمِينَ ﴾
[آل عِمران: 125]

“Inde, ngati inu mupirira ndi kukhala angwiro ndipo pamene mdani adza mofulumira kwa inu, Ambuye wanu adzakuthandizani ndi angelo zikwi zisanu a zizindikiro.”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: بلى إن تصبروا وتتقوا ويأتوكم من فورهم هذا يمددكم ربكم بخمسة آلاف, باللغة نيانجا

﴿بلى إن تصبروا وتتقوا ويأتوكم من فورهم هذا يمددكم ربكم بخمسة آلاف﴾ [آل عِمران: 125]

Khaled Ibrahim Betala
“Inde, ngati mupirira ndi kudziteteza ku machimo, ndipo (adani anu) nakudzerani mwachangu chawo chimenechi, pamenepo Mbuye wanu adzakuonjezerani ndi zikwi zisanu za angelo odziwa kumenya nkhondo.”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek