×

Ndipo fulumirani kukapeza chikhululukiro cha Ambuye wanu ndi Paradiso imene kutambasuka kwake 3:133 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah al-‘Imran ⮕ (3:133) ayat 133 in Chichewa

3:133 Surah al-‘Imran ayat 133 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah al-‘Imran ayat 133 - آل عِمران - Page - Juz 4

﴿۞ وَسَارِعُوٓاْ إِلَىٰ مَغۡفِرَةٖ مِّن رَّبِّكُمۡ وَجَنَّةٍ عَرۡضُهَا ٱلسَّمَٰوَٰتُ وَٱلۡأَرۡضُ أُعِدَّتۡ لِلۡمُتَّقِينَ ﴾
[آل عِمران: 133]

Ndipo fulumirani kukapeza chikhululukiro cha Ambuye wanu ndi Paradiso imene kutambasuka kwake kuli ngati kumwamba ndi dziko lapansi, yokonzedwera anthu oopa Mulungu

❮ Previous Next ❯

ترجمة: وسارعوا إلى مغفرة من ربكم وجنة عرضها السموات والأرض أعدت للمتقين, باللغة نيانجا

﴿وسارعوا إلى مغفرة من ربكم وجنة عرضها السموات والأرض أعدت للمتقين﴾ [آل عِمران: 133]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndipo chimkereni mwachangu chikhululuko cha Mbuye wanu (kupyolera m’zochita zanu zabwino), ndi Munda (Wake) umene Kutambasuka kwake (mulifupi) kuli ngati kumwamba ndi pansi, (womwe) wakonzedwa kuti ukhale wa oopa Allah
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek