×

Ngati inu muvulala, zindikirani kuti ena nawo adavulala. Ndipo masiku sakoma onse 3:140 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah al-‘Imran ⮕ (3:140) ayat 140 in Chichewa

3:140 Surah al-‘Imran ayat 140 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah al-‘Imran ayat 140 - آل عِمران - Page - Juz 4

﴿إِن يَمۡسَسۡكُمۡ قَرۡحٞ فَقَدۡ مَسَّ ٱلۡقَوۡمَ قَرۡحٞ مِّثۡلُهُۥۚ وَتِلۡكَ ٱلۡأَيَّامُ نُدَاوِلُهَا بَيۡنَ ٱلنَّاسِ وَلِيَعۡلَمَ ٱللَّهُ ٱلَّذِينَ ءَامَنُواْ وَيَتَّخِذَ مِنكُمۡ شُهَدَآءَۗ وَٱللَّهُ لَا يُحِبُّ ٱلظَّٰلِمِينَ ﴾
[آل عِمران: 140]

Ngati inu muvulala, zindikirani kuti ena nawo adavulala. Ndipo masiku sakoma onse ndipo Ife timapereka kwa anthu mwakasintha sintha kuti Mulungu ayese iwo amene akhulupirira ndipo kuti akhoza kupha ena kuchokera ku magulu anu. Ndipo Mulungu sakonda iwo amene amachita zoipa

❮ Previous Next ❯

ترجمة: إن يمسسكم قرح فقد مس القوم قرح مثله وتلك الأيام نداولها بين, باللغة نيانجا

﴿إن يمسسكم قرح فقد مس القوم قرح مثله وتلك الأيام نداولها بين﴾ [آل عِمران: 140]

Khaled Ibrahim Betala
“Ngati mwavulazidwa, naonso anthuwo avulazidwanso molingana. Ndipo amenewo ndimasiku, timawapatsa anthu mosinthanasinthana. (Ichi chachitika) kuti Allah aonetse poyera amene akhulupirira (moona; choncho sadathawe konse); ndi kuti awachite ena mwa inu kukhala Shuhadaa (ofera pankhondo yoyera). Komatu Allah sakonda anthu ochita zoipa
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek