×

Iwo amasangalala chifukwa cha zimene Mulungu wawapatsa mwa chisomo chake ndi chifukwa 3:170 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah al-‘Imran ⮕ (3:170) ayat 170 in Chichewa

3:170 Surah al-‘Imran ayat 170 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah al-‘Imran ayat 170 - آل عِمران - Page - Juz 4

﴿فَرِحِينَ بِمَآ ءَاتَىٰهُمُ ٱللَّهُ مِن فَضۡلِهِۦ وَيَسۡتَبۡشِرُونَ بِٱلَّذِينَ لَمۡ يَلۡحَقُواْ بِهِم مِّنۡ خَلۡفِهِمۡ أَلَّا خَوۡفٌ عَلَيۡهِمۡ وَلَا هُمۡ يَحۡزَنُونَ ﴾
[آل عِمران: 170]

Iwo amasangalala chifukwa cha zimene Mulungu wawapatsa mwa chisomo chake ndi chifukwa cha iwo amene sadalowe mgulu lawo ndipo anatsala m’mbuyo, ndipo iwo sadzakhala ndi mantha kapena kumva chisoni

❮ Previous Next ❯

ترجمة: فرحين بما آتاهم الله من فضله ويستبشرون بالذين لم يلحقوا بهم من, باللغة نيانجا

﴿فرحين بما آتاهم الله من فضله ويستبشرون بالذين لم يلحقوا بهم من﴾ [آل عِمران: 170]

Khaled Ibrahim Betala
“Akukondwera pa zimene wawapatsa Allah kuchokera m’zabwino Zake. Ndipo akufunira mafuno abwino amene sadakumane nawo omwe ali pambuyo pawo, (omwe alipobe pa dziko lapansi) ponena kuti pa iwo sipadzakhala mantha kapena kudandaula
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek