×

Ndithudi chipembedzo cha Mulungu ndi Chisilamu. Iwo amene adapatsidwa Buku sadagawikane pa 3:19 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah al-‘Imran ⮕ (3:19) ayat 19 in Chichewa

3:19 Surah al-‘Imran ayat 19 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah al-‘Imran ayat 19 - آل عِمران - Page - Juz 3

﴿إِنَّ ٱلدِّينَ عِندَ ٱللَّهِ ٱلۡإِسۡلَٰمُۗ وَمَا ٱخۡتَلَفَ ٱلَّذِينَ أُوتُواْ ٱلۡكِتَٰبَ إِلَّا مِنۢ بَعۡدِ مَا جَآءَهُمُ ٱلۡعِلۡمُ بَغۡيَۢا بَيۡنَهُمۡۗ وَمَن يَكۡفُرۡ بِـَٔايَٰتِ ٱللَّهِ فَإِنَّ ٱللَّهَ سَرِيعُ ٱلۡحِسَابِ ﴾
[آل عِمران: 19]

Ndithudi chipembedzo cha Mulungu ndi Chisilamu. Iwo amene adapatsidwa Buku sadagawikane pa chifukwa china chili chonse koma nsanje pamene nzeru zidadza kwa iwo. Ndipo aliyense amene akana zizindikiro za Mulungu, ndithudi, Mulungu ndi wachangu polanga

❮ Previous Next ❯

ترجمة: إن الدين عند الله الإسلام وما اختلف الذين أوتوا الكتاب إلا من, باللغة نيانجا

﴿إن الدين عند الله الإسلام وما اختلف الذين أوتوا الكتاب إلا من﴾ [آل عِمران: 19]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndithudi, chipembedzo (choona) kwa Allah ndi Chisilamu. Ndipo amene adapatsidwa buku (Ayuda ndi Akhrisitu) sadatsutsane koma pambuyo powabwerera kuzindikira. (Adatsutsana) chifukwa cha dumbo lomwe lidali pakati pawo. Ndipo amene akukana zisonyezo za Allah, (Allah akamulanga pa tsiku la chiweruziro). Ndithu Allah Ngwachangu powerengera
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek