×

oh inu anthu okhulupirira! Pilirani ndipo khalani opirira kwambiri ndipo tetezani dziko 3:200 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah al-‘Imran ⮕ (3:200) ayat 200 in Chichewa

3:200 Surah al-‘Imran ayat 200 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah al-‘Imran ayat 200 - آل عِمران - Page - Juz 4

﴿يَٰٓأَيُّهَا ٱلَّذِينَ ءَامَنُواْ ٱصۡبِرُواْ وَصَابِرُواْ وَرَابِطُواْ وَٱتَّقُواْ ٱللَّهَ لَعَلَّكُمۡ تُفۡلِحُونَ ﴾
[آل عِمران: 200]

oh inu anthu okhulupirira! Pilirani ndipo khalani opirira kwambiri ndipo tetezani dziko lanu poika Asirikari pamalo okhazikika pamene adani anu akhoza kudzera, ndipo muope Mulungu kuti mukhoza kukhala opambana

❮ Previous Next ❯

ترجمة: ياأيها الذين آمنوا اصبروا وصابروا ورابطوا واتقوا الله لعلكم تفلحون, باللغة نيانجا

﴿ياأيها الذين آمنوا اصبروا وصابروا ورابطوا واتقوا الله لعلكم تفلحون﴾ [آل عِمران: 200]

Khaled Ibrahim Betala
“E inu amene mwakhulupirira! Pirirani, ndipo agonjetseni adani anu ndikupirirako; ndipo tetezani malire anu ndipo muopeni Allah kuti mukhale opambana
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek