×

Ndipo iye sangakulamuleni kuti musandutse Angelo ndi Atumwi ngati milungu yanu ayi. 3:80 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah al-‘Imran ⮕ (3:80) ayat 80 in Chichewa

3:80 Surah al-‘Imran ayat 80 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah al-‘Imran ayat 80 - آل عِمران - Page - Juz 3

﴿وَلَا يَأۡمُرَكُمۡ أَن تَتَّخِذُواْ ٱلۡمَلَٰٓئِكَةَ وَٱلنَّبِيِّـۧنَ أَرۡبَابًاۚ أَيَأۡمُرُكُم بِٱلۡكُفۡرِ بَعۡدَ إِذۡ أَنتُم مُّسۡلِمُونَ ﴾
[آل عِمران: 80]

Ndipo iye sangakulamuleni kuti musandutse Angelo ndi Atumwi ngati milungu yanu ayi. Kodi iye akhoza kukulamulirani inu kuti mukhale anthu osakhulupirira pamene inu mwadzipereka kale kwa Mulungu

❮ Previous Next ❯

ترجمة: ولا يأمركم أن تتخذوا الملائكة والنبيين أربابا أيأمركم بالكفر بعد إذ أنتم, باللغة نيانجا

﴿ولا يأمركم أن تتخذوا الملائكة والنبيين أربابا أيأمركم بالكفر بعد إذ أنتم﴾ [آل عِمران: 80]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndipo sangakulamulireni kuwasandutsa angelo ndi aneneri kukhala milungu. Kodi angakulamulireni kusakhulupirira pambuyo poti muli Asilamu (ogonjera)
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek