×

Koma patsiku limeneli zodandaula zawo sizidzawathandiza anthu onse ochimwa ndipo sizidzamveka ayi 30:57 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Ar-Rum ⮕ (30:57) ayat 57 in Chichewa

30:57 Surah Ar-Rum ayat 57 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Ar-Rum ayat 57 - الرُّوم - Page - Juz 21

﴿فَيَوۡمَئِذٖ لَّا يَنفَعُ ٱلَّذِينَ ظَلَمُواْ مَعۡذِرَتُهُمۡ وَلَا هُمۡ يُسۡتَعۡتَبُونَ ﴾
[الرُّوم: 57]

Koma patsiku limeneli zodandaula zawo sizidzawathandiza anthu onse ochimwa ndipo sizidzamveka ayi

❮ Previous Next ❯

ترجمة: فيومئذ لا ينفع الذين ظلموا معذرتهم ولا هم يستعتبون, باللغة نيانجا

﴿فيومئذ لا ينفع الذين ظلموا معذرتهم ولا هم يستعتبون﴾ [الرُّوم: 57]

Khaled Ibrahim Betala
“Choncho tsiku limenelo, madandaulo a omwe adzichitira chinyengo sadzawathandiza ndipo sadzafunsidwa kuti amukondweretse Allah (ndi kulapa kwawo)
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek