×

Nena, “Ine ndili kukufunsani kuti muchite chinthu chimodzi choti muime pamaso pa 34:46 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Saba’ ⮕ (34:46) ayat 46 in Chichewa

34:46 Surah Saba’ ayat 46 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Saba’ ayat 46 - سَبإ - Page - Juz 22

﴿۞ قُلۡ إِنَّمَآ أَعِظُكُم بِوَٰحِدَةٍۖ أَن تَقُومُواْ لِلَّهِ مَثۡنَىٰ وَفُرَٰدَىٰ ثُمَّ تَتَفَكَّرُواْۚ مَا بِصَاحِبِكُم مِّن جِنَّةٍۚ إِنۡ هُوَ إِلَّا نَذِيرٞ لَّكُم بَيۡنَ يَدَيۡ عَذَابٖ شَدِيدٖ ﴾
[سَبإ: 46]

Nena, “Ine ndili kukufunsani kuti muchite chinthu chimodzi choti muime pamaso pa Mulungu awiriawiri kapena aliyense payekha ndipo muganize painu nokha. M’bale wanu si wamisala ayi. Iye ali kungokuchenjezani chilango chowawa chisanadze.”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: قل إنما أعظكم بواحدة أن تقوموا لله مثنى وفرادى ثم تتفكروا ما, باللغة نيانجا

﴿قل إنما أعظكم بواحدة أن تقوموا لله مثنى وفرادى ثم تتفكروا ما﴾ [سَبإ: 46]

Khaled Ibrahim Betala
“Nena: “Ndithu ndikukulangizani chinthu chimodzi, kuti muimilire chifukwa cha Allah; awiriawiri ndi mmodzimmodzi, ndipo kenako mulingalire; (muona kuti uyu Muhammad {s.a.w} chilichonse chomwe akunena nchoona. Ndiponso muona kuti) mnzanuyu alibe misala. Iye, sichina, koma ndimchenjezi wanu chisanadze chilango chaukali.”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek