×

Ndipo dziko lapansi lidzawala ndi muuni wa Ambuye wako ndipo Buku lidzatsekulidwa. 39:69 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Az-Zumar ⮕ (39:69) ayat 69 in Chichewa

39:69 Surah Az-Zumar ayat 69 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Az-Zumar ayat 69 - الزُّمَر - Page - Juz 24

﴿وَأَشۡرَقَتِ ٱلۡأَرۡضُ بِنُورِ رَبِّهَا وَوُضِعَ ٱلۡكِتَٰبُ وَجِاْيٓءَ بِٱلنَّبِيِّـۧنَ وَٱلشُّهَدَآءِ وَقُضِيَ بَيۡنَهُم بِٱلۡحَقِّ وَهُمۡ لَا يُظۡلَمُونَ ﴾
[الزُّمَر: 69]

Ndipo dziko lapansi lidzawala ndi muuni wa Ambuye wako ndipo Buku lidzatsekulidwa. Atumwi ndi mboni zidzaitanidwa ndipo chiweruzo chidzaperekedwa mwachilungamo pakati pawo ndipo iwo sadzaponderezedwa konse

❮ Previous Next ❯

ترجمة: وأشرقت الأرض بنور ربها ووضع الكتاب وجيء بالنبيين والشهداء وقضي بينهم بالحق, باللغة نيانجا

﴿وأشرقت الأرض بنور ربها ووضع الكتاب وجيء بالنبيين والشهداء وقضي بينهم بالحق﴾ [الزُّمَر: 69]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndipo nthaka (tsiku limenelo) idzawala ndi kuunika kwa Mbuye wake; ndipo akaundula a zochita, adzaikidwa. Ndipo adzabweretsedwa aneneri ndi mboni (kuti aikire umboni pa anthu). Ndipo padzaweruzidwa pakati pawo mwachoonadi; ndipo iwo sadzaponderezedwa
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek